1
MARKO 2:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo pamene Yesu anamva ichi, ananena nao, Akulimba safuna sing'anga, koma odwala ndiwo; sindinadza kudzaitana olungama, koma ochimwa.
താരതമ്യം
MARKO 2:17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MARKO 2:5
Ndipo Yesu pakuona chikhulupiriro chao ananena ndi wodwala manjenje, Mwana, machimo ako akhululukidwa.
MARKO 2:5 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MARKO 2:27
Ndipo ananena nao, Sabata linaikidwa chifukwa cha munthu, si munthu chifukwa cha Sabata
MARKO 2:27 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MARKO 2:4
Ndipo pamene sanakhoze kufika kuli Iye, chifukwa cha khamu la anthu, anasasula chindwi pokhala Iye; ndipo pamene anatha kuliboola, anatsitsa mphasa m'mene alinkugonamo wodwala manjenjeyo.
MARKO 2:4 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MARKO 2:10-11
Koma kuti mudziwe kuti Mwana wa Munthu ali mwini ulamuliro wakukhululukira machimo pa dziko lapansi (ananena ndi wodwala manjenje), Ndikuuza iwe, Nyamuka, senza mphasa yako, numuke kwanu.
MARKO 2:10-11 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MARKO 2:9
Chapafupi nchiti, kuuza wodwala manjenje kuti, Machimo ako akhululukidwa; kapena kuti, Nyamuka, senza mphasa yako, nuyende?
MARKO 2:9 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
MARKO 2:12
Ndipo ananyamuka iye pomwepo, nasenza mphasa, natuluka pamaso pa iwo onse; kotero kuti anadabwa onse, nalemekeza Mulungu, nanena kuti, Zotere sitinaziona ndi kale lonse.
MARKO 2:12 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ