YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

Matayo 2の有名な聖句

1

Matayo 2:11

Nyanja

NTNYBL2025

Ndiipo adalowa mnyumba ni adamuona mwana pamojhi ni Maliya maye wake. Adagwada ni kumlambila. Adamasula mbhaso zao ni kumpacha mwana zaabu ni ubani ni mnghwala uwo utanidwa manemane.

比較

Matayo 2:11で検索

2

Matayo 2:1-2

Nyanja

NTNYBL2025

Yesu wadabadwa ku mujhi wa Beselehemu mjhiko la Yudea. Ndhawi imeneyo Helode wadali mfumu. Yesu yapo wadandobadwa wandhu yawo amajhiwa icho sichichokele adafika ku Yelusalemu adaafunjha, “Walikuti mwana uyo wabadwa Mfumu wa Ayahudi? Pakuti tayiona ndhondwa yake kudela la kumwela ni nafenjho tajha kumulambila.”

比較

Matayo 2:1-2で検索

3

Matayo 2:10

Nyanja

NTNYBL2025

Yapo adaiona ndhondwa ijha adakondwa kupunda.

比較

Matayo 2:10で検索

4

Matayo 2:12-13

Nyanja

NTNYBL2025

Ndiipo Mnungu adaonya kumaloto kuti asadabwelela kwa Helode. Chimwecho adabwela kujhiko lawo kwa kupitila njila yina. Wandhu yapo adatochoka mtumiki wa Ambuye wadamujhela Yusufu kumaloto ni kumkambila kuti, “Nyamuka umutenge mwana ni maye wake mthawile Kumisili. Mkakhale kumweko mbaka yapo sinikukambile pakuti Helode wafuna kuti wamphe mwanayo.”

比較

Matayo 2:12-13で検索

無料の読書プランとMatayo 2に関係したデボーション

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ