1
Matayo 3:8
Nyanja
NTNYBL2025
Mchite vichito vijha vilangiza kuti mwayasiya machimo yanu.
比較
Matayo 3:8で検索
2
Matayo 3:17
Mwachizulumukila mvekelo kuchokela kumwamba udaveka, “Uyu nde Mwana wanga wokondedwa uyo nikondwela nayo.”
Matayo 3:17で検索
3
Matayo 3:16
Pampajha, Yesu yapo wadamaliza kubatizidwa wadachuuka mmajhi. Kumwamba kudamasuka ni wadaona Mzimu wa Mnungu niuchika ngati nghunda ni kutula pamwamba pake.
Matayo 3:16で検索
4
Matayo 3:11
Ine nikubatizani kwa majhi kulangiza kuti mwayasiya machimo yanu. Nambho uyo wakujha mmbuyo mwanga wali ni mbhamvu kupitilila ine. Ine sinifunika kutenga vingwe va malapasi yake. Iye siwakubatizeni kwa Mzimu Woyela ni moto.
Matayo 3:11で検索
5
Matayo 3:10
Basi nghwangwa yathoikidwa kudula mizo. Chimwecho mtengo uliwonjhe uwo suubala vipacho vabwino suudulidwe ni kutayidwa pamoto.
Matayo 3:10で検索
6
Matayo 3:3
Uyu nde Yohana yujha nghani zake zidakambidwa ni mlosi Isaya kuti, “Mundhu watana ku phululu, ‘Akonjeleni Ambuye njila yao tambasulani njila yake!’”
Matayo 3:3で検索
ホーム
聖書
読書プラン
ビデオ