YouVersion-ի լոգոն
ԱստվածաշունչԾրագրերՏեսանյութեր
Տեղադրեք հավելվածը
Ընտրել լեզուն
Որոնման պատկերակ

Աստվածաշնչի հայտնի հատվածներ GENESIS 12-ից

1

GENESIS 12:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo ndidzakuyesa iwe mtundu waukulu, ndipo ndidzakudalitsa iwe, ndi kubukitsa dzina lako; nukhale iwe mdalitso; ndipo ndidzadalitsa amene akudalitsa iwe; ndi kutemberera iye amene akutemberera iwe; ndipo mwa iwe adzadalitsidwa mabanja onse a dziko lapansi.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 12:2-3

2

GENESIS 12:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, Tuluka iwe m'dziko lako, ndi kwa abale ako, ndi kunyumba ya atate wako, kunka ku dziko limene ndidzakusonyeza iwe

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 12:1

3

GENESIS 12:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anamuka Abramu monga Yehova ananena kwa iye, ndipo Loti anamuka pamodzi naye: ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi awiri kudza zisanu, pamene anatuluka m'Harani.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 12:4

4

GENESIS 12:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anaonekera kwa Abramu nati, Ndidzapatsa mbeu yako dziko lino: pamenepo anammangira Yehova guwa la nsembe amene anamuonekera iye.

Համեմատել

Ուսումնասիրեք GENESIS 12:7

Նախորդ գլուխը
Հաջորդ գլուխը
YouVersion

Քաջալերում և մարտահրավեր ենք նետում Ձեզ Աստծո հետ մտերմանալու համար։

Ծառայություն

Մեր մասին

Աշխատատեղեր

Կամավոր

Բլոգ

Մամուլ

Օգտակար հղումներ

Օգնություն

Նվիրաբերել

Աստվածաշնչի տարբերակներ

Աուդիո Աստվածաշնչեր

Աստվածաշնչի լեզուներ

Օրվա խոսքը


Թվային ծառայություն

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Գաղտնիության քաղաքականությունՊայմանները
Խոցելիության բացահայտման ծրագիր
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Գլխավոր

Աստվածաշունչ

Ծրագրեր

Տեսանյութեր