1
Maluko 1:35
Nyanja
NTNYBL2025
Umawamawa siku lidachatila, Yesu wadapita kubwalo kwa mujhi, pamalo yapo padalibe wandhu, kumeneko wadampembha Mnungu.
Konpare
Eksplore Maluko 1:35
2
Maluko 1:15
Wadakamba, “Nyengo ya Mnungu yakwana yolamulila wandhu. Lapani ni kukhulupilila Uthenga Wabwino.”
Eksplore Maluko 1:15
3
Maluko 1:10-11
Yesu yapo wadachuuka mmajhi, pamwepo wadaona kumwamba kwamasulidwa, ni Mzimu Woyela udamchikila ngati nghunda. Mvekelo wa Mnungu udaveka kuchokela kumwamba, niukamba, “Iwe nde mwana wanga uyo nikukonda, nikondelechedwa ni iwe.”
Eksplore Maluko 1:10-11
4
Maluko 1:8
Ine nikubatizani kwa majhi, nambho iye siwakubatizeni kwa Mzimu Woyela.”
Eksplore Maluko 1:8
5
Maluko 1:17-18
Yesu wadaakambila, “Nichateni, nane sinikuyaluzeni mukhale owapeleka wandhu kwa ine, ngati umo mmavuwila njhomba.” Pampajha adavisia vilepa vao nikumchata.
Eksplore Maluko 1:17-18
6
Maluko 1:22
Wandhu yawo adamvela mayaluzo yake, adazizwa ndande siwamayaluze ngati umo amayaluzila oyaluza athauko la Musa, nambho iye wamayaluza ngati mundhu wa ulamulilo.
Eksplore Maluko 1:22
Akèy
Bib
Plan yo
Videyo