Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

Matayo 11

11
Yohana mbatizi waatuma oyaluzidwa wake kwa Yesu
Luka 7:18-35
1Yesu yapowadamaliza kwaapacha maagizo oyaluzidwa khumi ni awili, wadachokapo pamenepo, wadapita kuyaluza ni kulalikila wandhu amijhi ya jhiko la Galilaya.
2Yohana Mbatizi yapo wadali mndende wadavela vindhu ivo wamachita Kilisito. Yohana wadaatuma oyaluzidwa wake akamfunjhe, 3“Bwanji, iwe nde yujha wadakamba Yohana wakujha, kapina tumlinde mwina?”
4Yesu wadaayangha, “Pitani ni mkamkambile Yohana yayo mwayaona ni kuyavela. 5Osapenya apenya, viwete ayenda, amakate alamichidwa, osavela avela, akufa ahyukichidwa ni osauka alalikidwa Uthenga wa Bwino. 6Ali ni mwawi wandhu yawo sianikhaikila ine.”
7Oyaluzidwa a Yohana yapo amachoka, Yesu wadalifunjha gulu la wandhu nghani za Yohana mbatizi, “Mdapita kuphululu kupenya chiyani? Bwanji, mdafuna kupenya ujhu nilitingizidwa ni mbhepo? 8Ngati osati chimwecho, chipano mdapita kuona chiyani? Mdapita kumwona mundhu wavala njhalu zabwino? Wandhu yawo avala njhalu zabwino akhala mnyumba za mafumu. 9Nikambileni, mdapita kupenya chiyani? Bwanji mdapita kumuona mlosi? Notho, nambho mdaona mundhu wamkulu kupitilila mlosi. 10Uyu nde Yohana uyo wadakambidwa mu Malembo Yoyela niwakamba, ‘Ine, nimtuma mthenga wanga wakuchogolele, uyo siwakukonjele njila.’ 11Zene nikukambilani, pakati pa wana wonjhe abalidwa ni wamkazi, siwadachokelepo mundhu wa mkulu kupitilila Yohana Mbatizi. Ata chimwecho, yujha wali wamng'ono kupunda mu ufumu wakumwamba ni wamkulu kupitilila Yohana. 12Kuyambila masiku ya Yohana Mbatizi yapo wamalalikila mbaka lelo, ufumu wa kumwamba uchuchana kwa mbhavu, ni yawo ali ni mbhavu nde yawo aulanda. 13Thauko la Musa ni mayaluzo yonjhe ya alosi yadakambilila nghani za ufumu wa Mnungu mbaka kujha kwa Yohana Mbatizi. 14Ngati muvomela, Yohana nde Elia uyo wakadajha. 15Uyo wali nimakutu yovela, wavele!”
16“Bwanji wandhu amasiku yano alingana ni chiyani? Alingana ni anyamata yawo akhala paliwala, yawo waatana achanjao ni kwaakambila, 17‘Takutimbilani chitolilo, nambho simudavine! Taimba zaya nambho simudalile!’ 18Yohana wadajha, wadamanga kudya ni kumwa, anyiiwo adakamba, ‘Wazamwa ni chiwanda!’ 19Mwana wa Mundhu wajha, niwadya ni kumwa, anyiiwo akamba, ‘Mpenyeni uyu waludyo ni olojhela, bwenji wa olandila malipilo ni amachimo!’ Ata chimwecho, njelu ya Mnungu ichimikizidwa zene ndande ya njhito zake.”
Mijhi ya wandhu osakhulupilila
Luka 10:13-15
20Ndiipo Yesu wadayamba kwaleswa wandhu amijhi iyo wadachita vodabwicha vambili, ndande wandhu wake siadalape. 21“Uli ni choka iwe Kolazini! Uli ni choka iwe Betisaida! Pakuti, vodabwicha ivo vachitika kwanu vidakachitika ku Tilo ni ku Sidoni, wandhu wake adakalapa ni kuvala maguniya ni kujinyeka vyoso kulangiza kuti alapa machimo yao. 22Nikukambilani, Mnungu siwakulangeni kupunda anyiimwe kupitilila wandhu amijhi ya Tilo ni Sidoni. 23Nawe Kapelinaumu, bwanji, uganiza kuti siunyakulidwe mbaka kumwamba? Siuchichidwe mbaka kujhiko la wandhu akufa! Ngati vodabwicha vachitika kwako vidakachitika ku Sodoma, mujhi umeneo udakakhalapo mbaka lelo. 24Nikukambila, pa siku la lamulo Mnungu siwakulangeni kupunda kupitilila wandhu aku Sodoma.”
Majhani kwanga mpumulile
Luka 10:21-22
25Ndhawi imweyo Yesu wadakamba, “Nikutamandani Atate, Ambuye a kumwamba ni pajhiko, pakuti mwaabisa wandhu anjelu ni wosoma vindu ivi, namwe mwavunukulila wandhu yawo ali ngati wana waang'ono. 26Yetu, Atate wanga, umu ndeumo mwakondela ichokele.”
27“Atate wanga anipacha vindu vonjhe. Palibe uyo wamjhiwa Mwana nambho Tate wakepe, ni walionjhe yujha Mwana wamsangha kumvunukulila kuti waajhiwe Atate.”
28“Majhani kwa ine, mwaonjhe mchauchika ni kuvutika ni makatundu yolemela, ine sinikuchiteni mpumulile. 29Jhichocheni kwa ine ni mnitumikile, mujhiyaluze kwanga, pakuti ine asati okalipa ni nilibe mbuli, namwenjho simpumulile. 30Pakuti, mayaluzo yayo nikupachani asati yolimba ni yopepuka.”

Actualmente seleccionado:

Matayo 11: NTNYBL2025

Destacar

Compartir

Copiar

None

¿Quieres tener guardados todos tus destacados en todos tus dispositivos? Regístrate o inicia sesión