YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 1:20

Mt. 1:20 BLY-DC

Akulingalira zimenezi, mngelo wa Ambuye adamuwonekera m'maloto, namuuza kuti, “Yosefe, mwana wa Davide, usaope kumtenga Maria, mkazi wakoyu. Pathupi ali napopa padachitika ndi mphamvu za Mzimu Woyera.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 1:20