Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Marko 8

1

Marko 8:35

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pakuti aliyense amene afuna kupulumutsa moyo wake adzawutaya, koma aliyense amene ataya moyo wake chifukwa cha Ine ndi cha Uthenga Wabwino, adzawupulumutsa.

Compara

Explorar Marko 8:35

2

Marko 8:36

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Kodi munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi, koma ndi kutaya moyo wake?

Compara

Explorar Marko 8:36

3

Marko 8:34

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Kenaka anayitana gulu la anthu pamodzi ndi ophunzira ake nati: “Ngati wina aliyense afuna kunditsata Ine, ayenera kudzikana yekha ndi kunyamula mtanda wake ndi kunditsata.

Compara

Explorar Marko 8:34

4

Marko 8:37-38

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Kapena nʼchiyani chomwe munthu angapereke chosinthana ndi moyo wake? Ngati wina achita manyazi chifukwa cha Ine ndi mawu anga mu mʼbado uno wachigololo ndi wochimwa, Mwana wa Munthu adzachita naye manyazi pamene adzabwera mu ulemerero wa Atate ake pamodzi ndi angelo oyera.”

Compara

Explorar Marko 8:37-38

5

Marko 8:29

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Iye anafunsa kuti, “Koma nanga inu, mumati ndine yani?” Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu.”

Compara

Explorar Marko 8:29

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Marko 8

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest