Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Marko 7

1

Marko 7:21-23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pakuti kuchokera mʼkati mwa mitima ya anthu, mumatuluka maganizo oyipa, chiwerewere, kuba, kupha, chigololo, dyera, nkhwidzi, chinyengo, machitidwe onyansa, kaduka, chipongwe, kudzikuza ndi kupusa. Zoyipa zonsezi zimatuluka mʼkati ndipo zimadetsa munthu.”

Compara

Explorar Marko 7:21-23

2

Marko 7:15

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Palibe kanthu kunja kwa munthu kamene kakalowa mwa iye kangamusandutse wodetsedwa. Koma zimene zituluka mwa munthu ndizo zimupanga kukhala wodetsedwa.”

Compara

Explorar Marko 7:15

3

Marko 7:6

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Iye anayankha kuti, “Yesaya ananena zoona pamene ananenera za inu achiphamaso; monga kunalembedwa kuti: “Anthu awa amandilemekeza Ine ndi milomo yawo, koma mitima yawo ili kutali ndi Ine.

Compara

Explorar Marko 7:6

4

Marko 7:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Amandilambira Ine kwachabe; ndi kuphunzitsa malamulo ndi malangizo a anthu.

Compara

Explorar Marko 7:7

5

Marko 7:8

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mwasiya malamulo a Mulungu ndipo mwagwiritsitsa miyambo ya anthu.”

Compara

Explorar Marko 7:8

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Marko 7

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest