Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Mateyu 3

1

Mateyu 3:8

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Onetsani chipatso cha kutembenuka mtima.

Compara

Explorar Mateyu 3:8

2

Mateyu 3:17

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye.”

Compara

Explorar Mateyu 3:17

3

Mateyu 3:16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu atangobatizidwa, nthawi yomweyo potuluka mʼmadzi, kumwamba kunatsekuka ndipo taonani, Mzimu wa Mulungu anatsika ngati nkhunda natera pa Iye.

Compara

Explorar Mateyu 3:16

4

Mateyu 3:11

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Ine ndikubatizani ndi madzi kusonyeza kutembenuka mtima. Koma pambuyo panga akubwera wina amene ali ndi mphamvu kuposa ine, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake. Iyeyu adzakubatizani ndi Mzimu Woyera ndi moto.

Compara

Explorar Mateyu 3:11

5

Mateyu 3:10

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Tikukamba pano nkhwangwa yayikidwa kale pa mizu ya mitengo, ndipo mtengo umene subala chipatso chabwino udulidwa ndi kuponyedwa pa moto.

Compara

Explorar Mateyu 3:10

6

Mateyu 3:3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Uyu ndi amene mneneri Yesaya ananena za iye kuti, “Mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.’ ”

Compara

Explorar Mateyu 3:3

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Mateyu 3

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest