1
Mateyu 3:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Onetsani chipatso cha kutembenuka mtima.
Compara
Explorar Mateyu 3:8
2
Mateyu 3:17
Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye.”
Explorar Mateyu 3:17
3
Mateyu 3:16
Yesu atangobatizidwa, nthawi yomweyo potuluka mʼmadzi, kumwamba kunatsekuka ndipo taonani, Mzimu wa Mulungu anatsika ngati nkhunda natera pa Iye.
Explorar Mateyu 3:16
4
Mateyu 3:11
“Ine ndikubatizani ndi madzi kusonyeza kutembenuka mtima. Koma pambuyo panga akubwera wina amene ali ndi mphamvu kuposa ine, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake. Iyeyu adzakubatizani ndi Mzimu Woyera ndi moto.
Explorar Mateyu 3:11
5
Mateyu 3:10
Tikukamba pano nkhwangwa yayikidwa kale pa mizu ya mitengo, ndipo mtengo umene subala chipatso chabwino udulidwa ndi kuponyedwa pa moto.
Explorar Mateyu 3:10
6
Mateyu 3:3
Uyu ndi amene mneneri Yesaya ananena za iye kuti, “Mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Konzani njira ya Ambuye, wongolani njira zake.’ ”
Explorar Mateyu 3:3