Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Mateyu 4

1

Mateyu 4:4

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anayankha kuti, “Zalembedwa, ‘Munthu sadzakhala ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu aliwonse ochokera mʼkamwa mwa Mulungu.’ ”

Compara

Explorar Mateyu 4:4

2

Mateyu 4:10

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anati kwa iye, “Choka Satana! Zalembedwa, ‘Pembedza Yehova Mulungu wako ndi kumutumikira Iye yekha.’ ”

Compara

Explorar Mateyu 4:10

3

Mateyu 4:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anamuyankha kuti, “Kwalembedwanso: ‘Musamuyese Yehova Mulungu wanu.’ ”

Compara

Explorar Mateyu 4:7

4

Mateyu 4:1-2

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pambuyo pake Yesu anatsogozedwa ndi Mzimu Woyera kupita ku chipululu kukayesedwa ndi mdierekezi. Ndipo atasala kudya masiku makumi anayi usana ndi usiku, anamva njala.

Compara

Explorar Mateyu 4:1-2

5

Mateyu 4:19-20

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anati, “Bwerani, tsateni Ine ndipo ndidzakusandutsani asodzi a anthu.” Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.

Compara

Explorar Mateyu 4:19-20

6

Mateyu 4:17

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Kuyambira nthawi imeneyo, Yesu anayamba kulalikira nati, “Tembenukani mtima ufumu wakumwamba wayandikira.”

Compara

Explorar Mateyu 4:17

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Mateyu 4

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest