Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Luka 2

1

Luka 2:11

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Lero mʼmudzi wa Davide wakubwadwirani Mpulumutsi; Iye ndi Khristu Ambuye.

Compara

Explorar Luka 2:11

2

Luka 2:10

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma mngeloyo anawawuza kuti, “Musachite mantha. Ine ndakubweretserani Uthenga Wabwino wachimwemwe chachikulu umene udzakhala wa anthu onse.

Compara

Explorar Luka 2:10

3

Luka 2:14

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Ulemerero kwa Mulungu mmwambamwamba, ndi mtendere kwa anthu pa dziko lapansi amene Iye akondwera nawo.”

Compara

Explorar Luka 2:14

4

Luka 2:52

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yesu anakula mu nzeru, msinkhu ndi chisomo cha Mulungu ndi anthu.

Compara

Explorar Luka 2:52

5

Luka 2:12

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ichi chidzakhala chizindikiro kwa inu: mukapeza mwana wakhanda wokutidwa ndi nsalu atagona modyera ngʼombe.”

Compara

Explorar Luka 2:12

6

Luka 2:8-9

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo kunali abusa amene amakhala ku dera lomwelo, kuyangʼanira ziweto zawo usiku. Mngelo wa Ambuye anaonekera kwa iwo ndipo ulemerero wa Ambuye unawala mowazungulira. Iwo anachita mantha.

Compara

Explorar Luka 2:8-9

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Luka 2

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest