Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Luka 1

1

Luka 1:37

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pakuti palibe chinthu chosatheka ndi Mulungu.”

Compara

Explorar Luka 1:37

2

Luka 1:38

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mariya anayankha kuti, “Ine ndine mtumiki wa Ambuye. Zikhale kwa ine monga mwanenera.”

Compara

Explorar Luka 1:38

3

Luka 1:35

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mngelo anayankha kuti, “Mzimu Woyera adzabwera pa iwe ndipo mphamvu ya Wammwambamwamba idzakuphimba, ndipo Woyerayo amene adzabadwe adzatchedwa Mwana wa Mulungu.

Compara

Explorar Luka 1:35

4

Luka 1:45

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Wodala iye amene wakhulupirira kuti chimene Ambuye wanena kwa iye chidzakwaniritsidwa!”

Compara

Explorar Luka 1:45

5

Luka 1:31-33

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Udzakhala woyembekezera ndipo udzabala mwana wamwamuna ndipo udzamupatse dzina loti Yesu. Iye adzakhala wamkulu ndipo adzatchedwa Mwana wa Wammwambamwamba. Ambuye Mulungu adzamupatsa Iye mpando waufumu wa abambo ake Davide, ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.”

Compara

Explorar Luka 1:31-33

6

Luka 1:30

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma mngeloyo anati kwa iye, “Usachite mantha Mariya, pakuti wapeza chisomo pamaso Mulungu.

Compara

Explorar Luka 1:30

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Luka 1

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest