YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 42 的热门经文

1

GENESIS 42:21

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo iwo anati wina ndi mnzake, Tachimwiratu mbale wathu, pamene tinaona kuvutidwa kwa mtima wake, potipembedzera ife, koma ife tinakana kumvera, chifukwa chake kuvutidwa kumene kwatifikira.

对照

探索 GENESIS 42:21

2

GENESIS 42:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anali wolamulira dziko; ndiye amene anagulitsa kwa anthu onse a m'dziko; ndipo anafika abale ake a Yosefe, namweramira pansi, nkhope zao pansi.

对照

探索 GENESIS 42:6

3

GENESIS 42:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anaona abale ake, ndipo anazindikira iwo, koma anadziyesetsa kwa iwo ngati mlendo, nanena kwa iwo mwankhanza: ndipo anati kwa iwo, Mufuma kuti inu? Nati iwo, Ku dziko la Kanani kudzagula chakudya.

对照

探索 GENESIS 42:7

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频