1
GENESIS 43:23
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo iye anati, Mtendere ukhale ndi inu, musaope; Mulungu wanu ndi Mulungu wa atate wanu anakupatsani inu chuma m'matumba anu; ine ndinali nazo ndalama zanu. Pamenepo anawatulutsira Simeoni.
对照
探索 GENESIS 43:23
2
GENESIS 43:30
Yosefe ndipo anafulumira, chifukwa mtima wake unakhumbitsa mphwake, ndipo anafuna polirira; nalowa m'chipinda chake naliramo.
探索 GENESIS 43:30
主页
圣经
计划
视频