YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 41 的热门经文

1

GENESIS 41:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.

对照

探索 GENESIS 41:16

2

GENESIS 41:38

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Farao anati kwa anyamata ake, Kodi ife tidzaone munthu ngati uyu, mzimu wa Mulungu uli m'mtima mwake?

对照

探索 GENESIS 41:38

3

GENESIS 41:39-40

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Popeza Mulungu wakuonetsa iwe zonsezo palibe wina wakuzindikira ndi wanzeru ngati iwe. Uziyang'anira pa nyumba yanga, ndipo anthu anga onse adzalamulidwa mwa mau ako; pa mpando wachifumu pokha ine ndidzakuposa iwe.

对照

探索 GENESIS 41:39-40

4

GENESIS 41:52

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga.

对照

探索 GENESIS 41:52

5

GENESIS 41:51

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anamutcha dzina la woyamba Manase, chifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zovuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga.

对照

探索 GENESIS 41:51

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频