YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 12 的热门经文

1

GENESIS 12:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo ndidzakuyesa iwe mtundu waukulu, ndipo ndidzakudalitsa iwe, ndi kubukitsa dzina lako; nukhale iwe mdalitso; ndipo ndidzadalitsa amene akudalitsa iwe; ndi kutemberera iye amene akutemberera iwe; ndipo mwa iwe adzadalitsidwa mabanja onse a dziko lapansi.

对照

探索 GENESIS 12:2-3

2

GENESIS 12:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, Tuluka iwe m'dziko lako, ndi kwa abale ako, ndi kunyumba ya atate wako, kunka ku dziko limene ndidzakusonyeza iwe

对照

探索 GENESIS 12:1

3

GENESIS 12:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anamuka Abramu monga Yehova ananena kwa iye, ndipo Loti anamuka pamodzi naye: ndipo Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi awiri kudza zisanu, pamene anatuluka m'Harani.

对照

探索 GENESIS 12:4

4

GENESIS 12:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anaonekera kwa Abramu nati, Ndidzapatsa mbeu yako dziko lino: pamenepo anammangira Yehova guwa la nsembe amene anamuonekera iye.

对照

探索 GENESIS 12:7

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频