YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 13 的热门经文

1

GENESIS 13:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

chifukwa kuti dziko lonse limene ulinkuona, ndidzakupatsa iwe ndi mbeu yako nthawi yonse.

对照

探索 GENESIS 13:15

2

GENESIS 13:14

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, atalekana naye Loti, Tukulatu maso ako, nuyang'anire kuyambira kumene uliko, kumpoto, ndi kumwera, ndi kum'mawa, ndi kumadzulo

对照

探索 GENESIS 13:14

3

GENESIS 13:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ndidzayesa mbeu yako monga fumbi lapansi: chotere kuti ngati munthu angathe kuwerenga fumbi lapansi, chomwechonso mbeu yako idzawerengedwa.

对照

探索 GENESIS 13:16

4

GENESIS 13:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Abramu anati kwa Loti, Tisachite ndeu, ine ndi iwe, abusa anga ndi abusa ako: chifukwa kuti ife ndife abale.

对照

探索 GENESIS 13:8

5

GENESIS 13:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Abramu anasuntha hema wake nafika nakhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure, imene ili m'Hebroni, nammangira Yehova kumeneko guwa la nsembe.

对照

探索 GENESIS 13:18

6

GENESIS 13:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Loti anatukula maso ake nayang'ana chigwa chonse cha Yordani kuti chonsecho chinali ndi madzi ambiri, asanaononge Yehova Sodomu ndi Gomora, monga munda wa Yehova, monga dziko la Ejipito pakunka ku Zowari.

对照

探索 GENESIS 13:10

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频