YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 11 的热门经文

1

GENESIS 11:6-7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati, Taonani, anthu ali amodzi, ndipo onse ali nacho chinenedwe chao chimodzi; ndipo ichi ayamba kuchita: ndipo tsopano palibe kanthu kakuletsedwa nao kamene akafuna kuchita. Tiyeni, titsike, pomwepo tisokoneze chinenedwe chao, kuti wina asamvere chinenedwe cha mnzake.

对照

探索 GENESIS 11:6-7

2

GENESIS 11:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Tiyeni, timange mudzi ndi nsanja, pamutu pake pafikire kumwamba; ndipo tidzipangire ife tokha dzina kuti tisabalalike pa dziko lonse lapansi.

对照

探索 GENESIS 11:4

3

GENESIS 11:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake anatcha dzina lake Babele; pakuti kumeneko Yehova anasokoneza chinenedwe cha dziko lonse lapansi; kuyambira pamenepo Yehova anabalalitsa iwo pa dziko lonse lapansi.

对照

探索 GENESIS 11:9

4

GENESIS 11:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi.

对照

探索 GENESIS 11:1

5

GENESIS 11:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mudzi ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.

对照

探索 GENESIS 11:5

6

GENESIS 11:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anabalalitsa iwo pa dziko lonse lapansi, ndipo analeka kumanga mudzi.

对照

探索 GENESIS 11:8

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频