1
Maluko 4:39-40
Nyanja
NTNYBL2025
Ndiipo Yesu wadauka ni kuunyindila mwela, “Khala chete!” Pampajha mwela udasiya ni nyanja idagona. Chimwecho Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, “Ndande yanji muopa? Bwanji, mkali mlibe chikulupililo?”
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Maluko 4:39-40
2
Maluko 4:41
Oyaluzidwa wake adaopa kupunda, adafunjhana, “Mundhu wa mtundu wanji uyu mbaka mwela umvela?”
Ṣàwárí Maluko 4:41
3
Maluko 4:38
Yesu wadali kumbuyo kwa lijha boti wadatogonela philo, oyaluzidwa wake adamuucha ni kumkambila, “Oyaluza, simganizila kuti ife titobila?”
Ṣàwárí Maluko 4:38
4
Maluko 4:24
Chinchijha wadaakambila, “Mkhale maso ni yayo muyavela. Chimchijha umo mujhichocha kuvechela mawu nde chimwecho Mnungu siwakuchite ulijhiwe mawu kupunda.
Ṣàwárí Maluko 4:24
5
Maluko 4:26-27
Yesu wadaendekela kukamba, “Ufumu wa Mnungu ulingati chimwechi. Mundhu mmojhi wadamijha mbewu mmunda. Usiku wamagona, ni usana wakhala maso, mbeu zimela ni kukula popande iye siwajhiwa icho chichitika.
Ṣàwárí Maluko 4:26-27
6
Maluko 4:23
Mchate icho mkambidwa!”
Ṣàwárí Maluko 4:23
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò