1
Maluko 3:35
Nyanja
NTNYBL2025
Mundhu waliwonjhe uyo wachita yayo wayafuna Mnungu, mmeneyo nde mkulu wanga ni mlongowanga ni maye wanga.”
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Maluko 3:35
2
Maluko 3:28-29
“Zenedi nikukambilani, machimo yonjhe yayo achita wandhu, ni kukafula kwawo konjhe, Mnungu siwalekelele. Nambho mundhu waliyonjhe uyo wamkafula Mzimu Woyela, kukafula kwake sikulekeleledwa muyaya. Ndande wachita machimo ya muyaya.”
Ṣàwárí Maluko 3:28-29
3
Maluko 3:24-25
Ufumu uliwonjhe ukapatukana ni kubulana, ufumu umenewo siukhoza kulimba. Ikakhala wandhu a nyumba imojhi apatukana achinawene magulumagulu yayo yachuchana, nyumba imeneyo siikhoza kulimba.
Ṣàwárí Maluko 3:24-25
4
Maluko 3:11
Wandhu yawo adali ni viwanda, yapo adamwona Yesu, adajhitaya panjhi pachogolo pake ni kukweza mvekelo, niakamba, “Iwe ni Mwana wa Mnungu!”
Ṣàwárí Maluko 3:11
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò