Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Levitiko 20

1

Levitiko 20:13

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Ngati munthu agonana ndi mwamuna mnzake ngati akugonana ndi mkazi, ndiye kuti onsewo achita chinthu cha manyazi. Choncho aphedwe. Magazi awo adzakhala pa mitu pawo.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 20:13

2

Levitiko 20:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Chifukwa chake dzipatuleni ndi kukhala woyera popeza Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 20:7

3

Levitiko 20:26

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Muzikhala woyera pamaso panga chifukwa Ine Yehova, ndine woyera ndipo ndakupatulani pakati pa anthu a mitundu yonse kuti mukhale anthu anga.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 20:26

4

Levitiko 20:8

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo sungani malangizo anga ndi kuwatsata. Ine ndine Yehova amene ndimakuyeretsani.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 20:8

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
Polski

©2026 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest