Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Levitiko 19

1

Levitiko 19:18

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Musamubwezere mnzanu choyipa kapena kumusungira kanthu kunkhosi, koma konda mnansi wako monga iwe mwini. Ine ndine Yehova.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 19:18

2

Levitiko 19:28

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Musadzichekecheke pathupi panu chifukwa cha munthu wakufa kapena kudzitema mphini pa thupi lanu. Ine ndine Yehova.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 19:28

3

Levitiko 19:2

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Uza gulu lonse la Aisraeli kuti, ‘Khalani oyera mtima chifukwa Ine, Yehova Mulungu wanu, ndine Woyera.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 19:2

4

Levitiko 19:17

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Musamude mʼbale wanu mu mtima mwanu. Koma mudzudzuleni mnzanu moona mtima kuti musakhale wolakwa.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 19:17

5

Levitiko 19:31

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Musamapite kwa woyankhula ndi mizimu ya anthu akufa, kapena kwa owombeza. Musamawafunefune kuti angakuyipitseni. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 19:31

6

Levitiko 19:16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“ ‘Musamapite uku ndi uku kunena bodza pakati pa anthu anu. “ ‘Musachite kanthu kalikonse kamene kangadzetse imfa kwa mnzanu. Ine ndine Yehova.

Porównaj

Przeglądaj Levitiko 19:16

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: Levitiko 19

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
Polski

©2026 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest