1
MARKO 1:35
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo m'mawa mwake anauka usikusiku, natuluka namuka kuchipululu, napemphera kumeneko.
താരതമ്യം
MARKO 1:35 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MARKO 1:15
nanena, Nthawi yakwanira, ndipo Ufumu wa Mulungu wayandikira; tembenukani mtima, khulupirirani Uthenga Wabwino.
MARKO 1:15 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MARKO 1:10-11
Ndipo pomwepo, alimkukwera potuluka m'madzi, anaona Iye thambo litang'ambika, ndi Mzimu alikutsikira pa Iye monga nkhunda: ndipo mau anatuluka m'thambo, Mwana wanga wokondedwa ndiwe, mwa Iwe ndikondwera bwino.
MARKO 1:10-11 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MARKO 1:8
Ndakubatizani inu ndi madzi; koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera.
MARKO 1:8 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MARKO 1:17-18
Ndipo Yesu ananena nao, Idzani pambuyo panga, ndipo ndidzakusandutsani inu asodzi a anthu. Ndipo pomwepo anasiya makoka ao, namtsata Iye.
MARKO 1:17-18 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MARKO 1:22
Ndipo anazizwa ndi chiphunzitso chake; pakuti anaphunzitsa monga mwini mphamvu, si monga alembi.
MARKO 1:22 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ