1
MATEYU 9:37-38
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pomwepo ananena kwa ophunzira ake, Zotuta zichulukadi koma antchito ali owerengeka. Chifukwa chake pempherani Mwini zotuta kuti akokose antchito kukututa kwake.
താരതമ്യം
MATEYU 9:37-38 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 9:13
Koma mukani muphunzire nchiyani ichi, Ndifuna chifundo, si nsembe ai; pakuti sindinadza kudzaitana olungama, koma ochimwa.
MATEYU 9:13 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 9:36
Koma Iye, poona makamuwo, anagwidwa m'mtima ndi chisoni chifukwa cha iwo, popeza anali okambululudwa ndi omwazikana, akunga nkhosa zopanda mbusa.
MATEYU 9:36 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 9:12
Ndipo m'mene Yesu anamva anati, Olimba safuna sing'anga ai, koma odwala.
MATEYU 9:12 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 9:35
Ndipo Yesu anayendayenda m'mizinda yonse ndi m'midzi, namaphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira Uthenga Wabwino wa Ufumuwo, nachiritsa nthenda iliyonse ndi zofooka zonse.
MATEYU 9:35 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ