1
MATEYU 8:26
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo ananena Iye kwa iwo, Muli amantha bwanji, okhulupirira pang'ono inu? Pomwepo Iye anauka, nadzudzula mphepo ndi nyanja, ndipo panagwa bata lalikulu.
താരതമ്യം
MATEYU 8:26 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 8:8
Koma kenturiyoyo anavomera nati, Ambuye, sindiyenera kuti mukalowe pansi pa chindwi langa iai; koma mungonena mau, ndipo adzachiritsidwa mnyamata wanga.
MATEYU 8:8 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 8:10
Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeza chikhulupiriro chotere.
MATEYU 8:10 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 8:13
Ndipo Yesu anati kwa kenturiyoyo, Pita, kukhale kwa iwe monga unakhulupirira. Ndipo anachiritsidwa mnyamatayo nthawi yomweyo.
MATEYU 8:13 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 8:27
Ndipo anazizwa anthuwo nanena, Ndiye munthu wotani uyu, pakuti ngakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?
MATEYU 8:27 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ