1
MATEYU 10:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.
താരതമ്യം
MATEYU 10:16 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 10:39
Iye amene apeza moyo wake, adzautaya; ndi iye amene ataya moyo wake, chifukwa cha Ine, adzaupeza.
MATEYU 10:39 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 10:28
Ndipo musamaopa amene akupha thupi, koma moyo sangathe kuupha; koma makamaka muope Iye, wokhoza kuononga moyo ndi thupi lomwe m'Gehena.
MATEYU 10:28 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 10:38
Ndipo iye amene satenga mtanda wake, natsata pambuyo panga, sayenera Ine.
MATEYU 10:38 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 10:32-33
Chifukwa chake yense amene adzavomereza Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamvomereza iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba. Koma yense amene adzandikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamkana iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba.
MATEYU 10:32-33 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MATEYU 10:8
Chiritsani akudwala, ukitsani akufa, konzani akhate, tulutsani ziwanda: munalandira kwaulere, patsani kwaulere.
MATEYU 10:8 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
MATEYU 10:31
Chifukwa chake musamaopa; inu mupambana mpheta zambiri.
MATEYU 10:31 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
8
MATEYU 10:34
Musalingalire kuti ndidadzera kuponya mtendere pa dziko lapansi; sindinadzera kuponya mtendere, koma lupanga.
MATEYU 10:34 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ