1
Maluko 10:45
Nyanja
NTNYBL2025
Ata, ine Mwana wa Mundhu sinidajhe kutumikilidwa, nambho kutumukila, ni kuchocha umoyo wanga kwa kwaombola wandhu ambili.”
Спореди
Истражи Maluko 10:45
2
Maluko 10:27
Yesu wadaapenyechecha ni kwaakambila, “Kwa mundhu siikhozekana, nambho kwa Mnungu ikhozekana, pakuti kila kandhu kwa Mnungu chikhozekana.”
Истражи Maluko 10:27
3
Maluko 10:52
Yesu wadamkambila, “Pita, kukhulupilila kwako kwakulamicha.” Pampajha, yujha sapenya wadakhoza kupenya, ndiipo wadamchata Yesu mnjila.
Истражи Maluko 10:52
4
Maluko 10:9
Chimwecho, icho wachilunjanicha Mnungu, mundhu siwadachisiyanicha.”
Истражи Maluko 10:9
5
Maluko 10:21
Yesu wadampenya ni wadamkonda, ni wadamkambila, “Wachepekeledwa ni chindhu chimojhi, pita ukaguliche kila chindhu ulinacho, ni ndalama izo siupate waapache wosauka, niiwe siukhale ni wopata kumwamba, ndiipo majha unichate.”
Истражи Maluko 10:21
6
Maluko 10:51
Yesu wadamfunjha, “Ufuna nikuchitile chiyani?” Sapenya yujha wadamuyangha, “Oyaluza, nipemhba nipenye.”
Истражи Maluko 10:51
7
Maluko 10:43
Nambho kwa anyiimwe siidakhala chimwecho, mundhu waliyonjhe uyo wafuna wakhale wamkulu, ifunika wakhale mbowa wa wonjhe.
Истражи Maluko 10:43
8
Maluko 10:15
Zenedi nikukambilani, mundhu waliyonjhe uyo siwaulandila Ufumu wa Mnungu ngati wana wang'onoang'ono umo aulandilila, siwalowelatu muufumu wa Mnungu.”
Истражи Maluko 10:15
9
Maluko 10:31
Nambho, yawo achogolela siakhale kumbuyo, ni akumbuyo siachogolele.”
Истражи Maluko 10:31
10
Maluko 10:6-8
Nambho, kuyambila kuumbidwa kwa jhiko, Mnungu wadaumba wamuna ni wamkazi. Chimwecho, wamuna siwasiye atate wake ni amake ni kulunjana ni mkazake, ni anyiiwo awili sakhale thupi limojhi. Chipano anyiiwo osati awilinjho, nambho ni thupi limojhi.
Истражи Maluko 10:6-8
Дома
Библија
Планови
Видеа