1
Matayo 17:20
Nyanja
NTNYBL2025
Yesu wadaayangha, “Ndande ya chikhulupi chanu chochepa. Nikukambilani uzene, ngati mdakakhala ni chikulupi ngati mbeu ya aladali, mdakakhoza kulikambila phili ili, ‘Chokapo upite yapo’ nalo udakapita. Palibe chindhu icho sichilepeleke kwanu.
Спореди
Истражи Matayo 17:20
2
Matayo 17:5
Petulo yapo wamakamba chimwecho, mtambo wong'azikila udavinikila, ni mvekelo udaveka kuchoka kumtambo, “Uyu nde Mwana wanga uyo nimkonda, nikondwela nayo kupunda, mveleni iye.”
Истражи Matayo 17:5
3
Matayo 17:17-18
Yesu wadaayangha, “Imwe mbadwa wopande chikhulupi ni olakwa! Sinikhale ni anyiimwe mbaka liti? Sinikulimbileni mtima mbaka liti? Jhinayoni pano mnyamatayo.” Ndiipo Yesu wadachinyindila chiwanda, nacho chidamchoka mnyamata, ni wadalama pampajha.
Истражи Matayo 17:17-18
Дома
Библија
Планови
Видеа