1
Matayo 5:15-16
Nyanja
NTNYBL2025
Wandhu saakweleza nyali ni kuikupika kwa debe. Nambho iyikidwa pamwamba poikila nyali kuti imulikile wandhu wonjhe yao ali mnyumba. Chimwecho dangalila lanu liwale pamaso pa wandhu kuti apenye vichito vanu vabwino ni kwaakweza Atate wanu akumwamba.”
比較
Matayo 5:15-16で検索
2
Matayo 5:14
“Anyiimwe ni dangalila la jhiko! Ni ngati nyumba iyo yamangidwa pamwamba pa phili siukhoza kubisika.
Matayo 5:14で検索
3
Matayo 5:8
“Ali ni mwawi yao ali ni mtima wabwino pakuti saamuone Mnungu.”
Matayo 5:8で検索
4
Matayo 5:6
“Ali ni mwawi yao afuna kupunda kuchita ivo vimkwadilicha Mnungu ndande Mnungu siwatangatile kuchita chimwecho.”
Matayo 5:6で検索
5
Matayo 5:44
Nambho ine nikukambilani akondeni adani wanu ni kwapembhela anyiyao akuvutichani anyiimwe
Matayo 5:44で検索
6
Matayo 5:3
“Ali ni mwawi wajha ajhiwa kuti amfuna Mnungu pakuti ufumu wa kumwamba ni wao.”
Matayo 5:3で検索
7
Matayo 5:9
“Ali ni mwawi wajha apeleka mtendele pakuti siatanidwe wana a Mnungu.”
Matayo 5:9で検索
8
Matayo 5:4
“Ali ni mwawi yao ali ni chisoni pakuti siathilidwe mtima.”
Matayo 5:4で検索
9
Matayo 5:10
“Ali ni mwayi anyiyao avutichidwa ndande ya kuchita yayo wafuna Mnungu Pakuti ufumu wa kumwamba ni wao!”
Matayo 5:10で検索
10
Matayo 5:7
“Ali ni mwawi wajha alengela wina lisungu pakuti Mnungu siwalengele lisungu.”
Matayo 5:7で検索
11
Matayo 5:11-12
“Muli ni mwawi wandhu yapo sakutukwaneni ni kukuvutichani ni kukunamizilani voipa ndande yanga. Kondwani ni lulutilani pakuti chikho chanu chachikulu chaikidwa kumwamba. Mchimwecho nde umo adaavuticha alosi akhale anyiimwe mkali wosabdwa.”
Matayo 5:11-12で検索
12
Matayo 5:5
“Ali ni mwawi yao ajhichicha pakuti Mnungu siwapache jhiko likhale lao.”
Matayo 5:5で検索
13
Matayo 5:13
“Anyiimwe ni mchele wa chinyope wa jhiko. Nambho mchele wa chinyopeo ngati wasukuluka sikomelechedwe ni chiyani? Ulibe njhito. Siutaidwe kubwalo nikupondedwa ni wandhu.”
Matayo 5:13で検索
14
Matayo 5:48
Chimwecho khalani wokwanila ngati Tate wanu wa kumwamba umo wali okwanila.”
Matayo 5:48で検索
15
Matayo 5:37
Ukakamba, ‘Yetu’ basi ikhale ‘Yetu.’ Ukakamba, ‘Notho’ basi ikhale ‘Notho.’ Chalichonjhe icho chipitilila nghani zimenezo chichoka kwa Woyesa.”
Matayo 5:37で検索
16
Matayo 5:38-39
“Mwavela kuti idakambidwa, ‘Diso kwa diso ni jhino kwa jhino.’ Nambho ine nikukambilani, msadabwezela mbwezo kwa mundhu uyo wakuchitila voipa. Mundhu wakakubula mbama kuchakaya la kwene chinchijha mleke wakubule chakaya lakawili.
Matayo 5:38-39で検索
17
Matayo 5:29-30
Ngati diso lako la kwene likakuchiticha kuti uchite chimo lizule ni kulitaya kutali. Mbasa kutaiza chiwalo chimojhi cha thupi lako kusiyana ni thupi lako lonjhe kutaidwa ku jehanamu ya moto. Ngati jhanja lako la kwene likuchiticha kuti uchite chimo lidule ni ukalitaye kutali ni iwe. Mbasa kutaiza chiwalo chimojhi cha thupi lako kusiyana ni thupi lako lonjhe kutaidwa ku jehanamu ya moto.”
Matayo 5:29-30で検索
ホーム
聖書
読書プラン
ビデオ