YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

Luka 19の有名な聖句

1

Luka 19:10

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pajatu Mwana wa Munthu anabwera kudzafunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.”

比較

Luka 19:10で検索

2

Luka 19:38

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Yodala mfumu imene ikubwera mʼdzina la Ambuye!” “Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!”

比較

Luka 19:38で検索

3

Luka 19:9

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anati kwa iye, “Lero chipulumutso chafika mʼnyumba ino, chifukwa munthu uyu nayenso ndi mwana wa Abrahamu.

比較

Luka 19:9で検索

4

Luka 19:5-6

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu atafika pa malopo, anayangʼana mmwamba ndipo anati kwa iye, “Zakeyu, tsika msangamsanga. Ine ndiyenera kukhala mʼnyumba mwako lero.” Ndipo nthawi yomweyo anatsika ndipo anamulandira mosangalala.

比較

Luka 19:5-6で検索

5

Luka 19:8

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma Zakeyu anayimirira ndipo anati kwa Ambuye, “Taonani Ambuye! Theka la chuma changa ndipereka kwa osauka ndipo ngati ndinamubera wina aliyense pa chilichonse, ndidzamubwezera mochulukitsa kanayi.”

比較

Luka 19:8で検索

6

Luka 19:39-40

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ena mwa Afarisi mʼgulumo anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, adzudzuleni ophunzira anu!” Iye anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani kuti, ngati atakhala chete, miyala idzafuwula.”

比較

Luka 19:39-40で検索

無料の読書プランとLuka 19に関係したデボーション

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ