Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MARKO 7

1

MARKO 7:21-23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti m'kati mwake mwa mitima ya anthu, mutuluka maganizo oipa, zachiwerewere, zakuba, zakupha, zachigololo, masiriro, zoipa, chinyengo, chinyanso, diso loipa, mwano, kudzikuza, kupusa: zoipa izi zonse zituluka m'kati, nizidetsa munthu.

Konpare

Eksplore MARKO 7:21-23

2

MARKO 7:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

kulibe kanthu kunja kwa munthu kukalowa mwa iye, kangathe kumdetsa: koma zinthu zakutuluka mwa munthu, ndizo zakumdetsa munthu.

Konpare

Eksplore MARKO 7:15

3

MARKO 7:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Iye ananena nao, Yesaya ananenera bwino za inu onyenga, monga mwalembedwa, Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao, koma mtima wao ukhala kutali ndi Ine.

Konpare

Eksplore MARKO 7:6

4

MARKO 7:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma andilambira Iye kwachabe, ndi kuphunzitsa maphunzitso, malangizo a anthu.

Konpare

Eksplore MARKO 7:7

5

MARKO 7:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.

Konpare

Eksplore MARKO 7:8

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MARKO 7

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo