Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MARKO 8

1

MARKO 8:35

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti yense wakufuna kupulumutsa moyo wake adzautaya; ndipo yense wakutaya moyo wake chifukwa cha Ine, ndi chifukwa cha Uthenga Wabwino, adzaupulumutsa.

Konpare

Eksplore MARKO 8:35

2

MARKO 8:36

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse, natayapo moyo wake?

Konpare

Eksplore MARKO 8:36

3

MARKO 8:34

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anadziitanira khamulo la anthu pamodzi ndi ophunzira ake, nati kwa iwo, Ngati munthu afuna kudza pambuyo panga, adzikanize yekha, nanyamule mtanda wake, nanditsate Ine.

Konpare

Eksplore MARKO 8:34

4

MARKO 8:37-38

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti munthu akapereka chiyani chosintha nacho moyo wake? Pakuti yense wakuchita manyazi chifukwa cha Ine, ndi cha mau anga mu mbadwo uno wachigololo ndi wochimwa, Mwana wa Munthu adzachitanso manyazi chifukwa cha iyeyu, pamene Iye adzafika nao angelo ake oyera, mu ulemerero wa Atate wake.

Konpare

Eksplore MARKO 8:37-38

5

MARKO 8:29

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Iye anawafunsa, Koma inu munena kuti ndine yani? Petro anayankha nanena naye, Ndinu Khristu.

Konpare

Eksplore MARKO 8:29

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MARKO 8

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo