Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan LUKA 2

1

LUKA 2:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

pakuti wakubadwirani inu lero, m'mudzi wa Davide, Mpulumutsi, amene ali Khristu Ambuye.

Konpare

Eksplore LUKA 2:11

2

LUKA 2:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mngelo anati kwa iwo, Musaope; pakuti onani, ndikuuzani inu uthenga wabwino wa chikondwero chachikulu, chimene chidzakhala kwa anthu onse

Konpare

Eksplore LUKA 2:10

3

LUKA 2:14

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ulemerero ukhale kwa Mulungu Kumwambamwamba, ndi mtendere pansi pano mwa anthu amene akondwera nao.

Konpare

Eksplore LUKA 2:14

4

LUKA 2:52

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anakulabe m'nzeru ndi mumsinkhu, ndi m'chisomo cha pa Mulungu ndi cha pa anthu.

Konpare

Eksplore LUKA 2:52

5

LUKA 2:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ichi ndi chizindikiro kwa inu: Mudzapeza mwana wakhanda wokuta ndi nsalu atagona modyera.

Konpare

Eksplore LUKA 2:12

6

LUKA 2:8-9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo panali abusa m'dziko lomwelo, okhala kubusa ndi kuyang'anira zoweta zao usiku. Ndipo mngelo wa Ambuye anaimirira pa awo, ndi kuwala kwa Ambuye kunawaunikira kozungulira: ndipo anaopa ndi mantha akulu.

Konpare

Eksplore LUKA 2:8-9

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak LUKA 2

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo