Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MACHITIDWE A ATUMWI 27

1

MACHITIDWE A ATUMWI 27:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake, limbikani mtima, amuna inu; pakuti ndikhulupirira Mulungu, kuti kudzatero monga momwe ananena ndi ine.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 27:25

2

MACHITIDWE A ATUMWI 27:23-24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti anaimirira kwa ine usiku walero mngelo wa Mulungu amene ndili wake, amenenso ndimtumikira, nanena, Usaope Paulo; ukaimirira pamaso pa Kaisara; ndipo, taona, Mulungu anakupatsa onse amene akuyenda nawe pamodzi.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 27:23-24

3

MACHITIDWE A ATUMWI 27:22

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma tsopano ndikuchenjezani mulimbike mtima; pakuti sadzatayika wamoyo mmodzi mwa inu, koma ngalawa ndiyo.

Konpare

Eksplore MACHITIDWE A ATUMWI 27:22

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MACHITIDWE A ATUMWI 27

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo