Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

Matayo 6

6
Nghani za kwaathangatila wandhu wina
1Yesu wadaendekela kukamba, “Mkhale maso msadachita vindhu vabwino pamaso pa wandhu kuti akuoneni. Ngati mchita chimwecho, Atate wanu ali kumwamba saakupachani chikho chalichonjhe.”
2“Ndiipo yapo umpacha osauka chindhu chilichonjhe usadauzila kwa wandhu. Usadachita ngati agunghuli umo achitila mnyumba yo komanilana Ayahudi ni mnjila kuti wandhu watamande. Zene nikukambilani achameneo atholandila chikho chao chonjhe. 3Nambho iwe yapo umthangatila osauka chita chimwecho ata mbwenji wako wa pafupi siwadajhiwa. 4Chindhu chimenecho sichikhale chisisi kwako, Atate wako yao apenya icho wachichita kwa chisisi siakupache chikho.”
Mayaluzo yopembhela
Luka 11:2-4
5“Yapo mpembhela msadalingana ni agunghuli. Anyiiwo akonda kuima ni kupembhela mnyumba ya mapembhelo yokomanilana Ayahudi ni mmalekano mwa mijhi kuti wandhu waaone. Zene nikukambilani achameneo athopata chikho chao. 6Nambho iwe yapo upembhela lowa kuchumba kwako cheka chicheko waapembhe Atate wako yawo saonekana. Ndiipo nawo Atate wako yawo ayaona yobisika siakupache chikho chako.”
7“Yapo upembhela usadakamba mawu yambili ngati wandhu yawo samjhiwa Mnungu. Anyiiwo aganiza kuti siwaavele ndande ya kuchuluka kwa mawu yawo. 8Usakhala ngati anyiiwo. Ndande Atate wanu achijhiwa chijha mchifuna ata ukali siudaapembhe. 9Nambho anyiimwe pembhelani chimwechi,
‘Atate wathu yawo muli kumwamba,
Jhina lanu likwezedwe.
10Ufumu wanu ujhe.
Ilo mlifuna lichitike pa jhiko lichitike ngati umo lichitikila kumwamba.
11Mtipache lelo chakudya chatu ngati umo mtipachila.
12Mtilekelele volakwa vathu
ngati ife umo talekelela yawo atilakwila.
13Msatiika mmayeso,
nambho utikengelele ni yujha Woipa.
Pakuti masiku yonjhe Ukulu ni wanu ni mbhavu ni ulemelelo mbaka muyaya. Amina.’ ”
14“Ngati mkaalekelela wandhu volakwa vao ivo akuchitilani, chinchijha Atate wanu aku mwamba siakulekeleleni volakwa vanu. 15Nambho ngati simwalekelela wandhu volakwa vao nawo Atate wanu a kumwamba siakulekelelani anyiimwe volakwa vanu.”
Yesu wayaluza kuusu kumanga
16Yesu wadaendekela kuyaluza, “Yapo mmanga simdalingana ni agunghuli yawo achita nghope zao zionekane kuti zili ni chisoni kuti aoneke amanga. Nikukambilani uzene achamenewo atholandila chikho chao. 17Yapo umanga usambe kumaso kwako ni unyeke mafuta mmutu mwako, 18kuti wandhu siwadajhiwa kuti wamanga kudya nambho ajhiwe Atate wakope yao saonekana. Nawo Atate wako yao aona yayo yabisika sakupache chikho.”
Kujhiikila chuma kumwamba
Luka 12:33-34
19“Msadajhiikila chuma chanu pajhiko yapo vidudu vowananga ni kutu viwananga ni anghungu akhoza kugomola ni kuba. 20Nambho jhiikileni chuma chanu kumwamba uko vidudu vowananga ni kutu sivikhoza kuwananga ni anghungu sakhoza kugomola ni kuba. 21Pakuti pajha pali chuma chako ndeyapo pali mtima wako.”
Nyali ya thupi
Luka 11:34-36
22“Maso nde nyali ya thupi. Ngati maso yako yali yabwino thupi lako lonjhe silikhalenjho mdangalila. 23Ngati maso yako yali yowanangika thupi lako lonjhe silikhale mumdima. Nambho ngati dangalila lali mkati mwako ni mdima basi uli muchimdima cha bii!”
Mnungu ni chuma
Luka 16:13; 12:22-31
24“Palibe wakhoza kutumikila wakulu awili. Pakuti siwamuipile mmojhi ni kumkonda mwina. Kapina siwavanichane ni mmojhi ni kumdelela mwina. Simukhoza kumtumikila Mnungu ni chuma kwa ndhawi imojhi.”
25“Ndendande nikukambilani msadajhichaucha pa umoyo wanu kuti simudye chiyani kapina simumwe chiyani kuti mkhale amoyo kapina mathupi yanu simuvale chiyani. Bwanji umoyo osati wa phindu kupitilila chakudya? Bwanji, thupi lilibe phindu kupitilila vivalo? 26Zipenyeni mbalami, sizivyala ni sizikolola ni alibe nghokwe yaliyonjhe. Nambho, Atate wanu akumwamba azidyecha. Bwanji, anyiimwe opande aphindu kupitilila mbalami? 27Yani pakati panu wakajhichaucha wakhoza kujhichuluchila ata saa limojhi la umoyo wake?”
28“Ndande yanji anyiimwe mjhichauchila vivalo? Yapenyeni maduwa ya mthengo umo yakulila. Siyachita njhito kapina kujhipotela viwalo. 29Nikukambilani, ata Solomoni mwenewake pa chuma chake chonjhe, siwadavekedwepo bwino ngati limojhi la maduwa yaya. 30Ngati, Mnungu wayaveka chimwecho machamba ya kuthengo yayo lelo yalipo ni mawa yathilidwa pamoto, bwanji, Mnungu siwakuvekani kupunda anyiimwe? Anyiimwe achikhulupi chochepa!”
31“Chimwecho, msadajhichaucha nimkamba, ‘Sitidye chiyani! Kapina sitimwe chiyani! Kapina sitivale chiyani!’ 32Pakuti yameneyo yonjhe wandhu yao siamjhiwa Mnungu ajhichauchila yaya yonjhe. Atate wanu akumwamba ajhiwa kuti mfuna ivi vonjhe. 33Chimwecho, ufuneni uti ufumu wa Mnungu ni kuchita yayo wayafuna Mnungu, ni iye siwakupacheni yaya yonjhe. 34Ndiipo, msadajhichauchila ya mawa, pakuti mawa siijhichauchile yeneyake. Kila siku lijhichauchila lene lake.”

Actualmente seleccionado:

Matayo 6: NTNYBL2025

Destacar

Compartir

Copiar

None

¿Quieres tener guardados todos tus destacados en todos tus dispositivos? Regístrate o inicia sesión