1
MALAKI 2:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti ndidana nako kuleka kumene, ati Yehova Mulungu wa Israele, ndi iye wakukuta chovala chake ndi chiwawa, ati Yehova wa makamu; chifukwa chake sungani mzimu wanu kuti musachite mosakhulupirika.
Comparar
Explorar MALAKI 2:16
2
MALAKI 2:15
Ndipo sanatero kodi wina womtsalira mzimu? Ndipo winayo anatero bwanji? Anatero pofuna mbeu ya Mulungu. Koma sungani mzimu wanu; ndipo asamchitire monyenga mkazi wa ubwana wake ndi mmodzi yense.
Explorar MALAKI 2:15
Inicio
Biblia
Planes
Vídeos