Logo de YouVersion
Icono de búsqueda

MALAKI 2:16

MALAKI 2:16 BLPB2014

Pakuti ndidana nako kuleka kumene, ati Yehova Mulungu wa Israele, ndi iye wakukuta chovala chake ndi chiwawa, ati Yehova wa makamu; chifukwa chake sungani mzimu wanu kuti musachite mosakhulupirika.

Planes de lectura y devocionales gratis relacionados con MALAKI 2:16