YouVersion-Logo
BibelLesepläneVideos
Hol dir die App!
Sprachauswahl
Suchsymbol

Beliebte Verse in LUKA 24

1

LUKA 24:49

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo onani, Ine nditumiza pa inu lonjezano la Atate wanga; koma khalani inu m'mudzi muno, kufikira mwavekedwa ndi mphamvu yochokera Kumwamba.

Vergleichen

Studiere LUKA 24:49

2

LUKA 24:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso m'Galileya

Vergleichen

Studiere LUKA 24:6

3

LUKA 24:31-32

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera. Ndipo anati wina kwa mnzake, Mtima wathu sunali wotentha m'kati mwathu nanga m'mene analankhula nafe m'njira, m'mene anatitsegulira malembo?

Vergleichen

Studiere LUKA 24:31-32

4

LUKA 24:46-47

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; ndi kuti kulalikidwe m'dzina lake kulapa ndi kukhululukidwa kwa machimo kwa mitundu yonse, kuyambira ku Yerusalemu.

Vergleichen

Studiere LUKA 24:46-47

5

LUKA 24:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Vergleichen

Studiere LUKA 24:2-3

Kostenlose Lesepläne und Andachten zum Thema LUKA 24

Vorheriges Kapitel
Nächstes Kapitel
YouVersion

Die App ermutigt und fordert dich heraus, jeden Tag die Gemeinschaft mit Gott zu suchen.

Dienst

Über

Jobangebote

Ehrenamtlich helfen

Blog

Presse

Nützliche Links

Hilfe

Spenden

Bibelübersetzungen

Hörbibeln

Bibelsprachen

Vers des Tages


Ein digitaler Dienst von

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

DatenschutzrichtlinieAGB
Verfahren zur Offenlegung von Sicherheitslücken (VDP)
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hauptbildschirm

Bibel

Lesepläne

Videos