Logo YouVersion
Ikona vyhledávání

LUKA 2:8-9

LUKA 2:8-9 BLPB2014

Ndipo panali abusa m'dziko lomwelo, okhala kubusa ndi kuyang'anira zoweta zao usiku. Ndipo mngelo wa Ambuye anaimirira pa awo, ndi kuwala kwa Ambuye kunawaunikira kozungulira: ndipo anaopa ndi mantha akulu.

Bezplatné plány čtení Bible a zamyšlení související s LUKA 2:8-9