1
EKSODO 36:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pamenepo anachita Bezalele ndi Oholiyabu, ndi anthu aluso, amene Yehova adaika luso ndi nzeru m'mtima mwao adziwe machitidwe ake a ntchito yonse ya utumiki wake wa malo opatulika, monga mwa zonse adauza Yehova.
Porovnat
Zkoumat EKSODO 36:1
2
EKSODO 36:3
Ndipo analandira kwa Mose chopereka chonse, chimene ana a Israele adabwera nacho chikhale cha machitidwe a ntchito ya malo opatulika, aipange nacho. Koma anaonjeza kubwera nazo kwa iye zopereka zaufulu, m'mawa ndi m'mawa.
Zkoumat EKSODO 36:3
Domů
Bible
Plány
Videa