1
EKSODO 26:33
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo uzitchinga nsalu yotchinga pa zokowerazo, nulowetse likasa la mboni kukati kwa nsalu yotchinga; ndipo nsalu yotchingayo idzakugawirani pakati pa malo opatulika ndi malo opatulika kwambiri.
Porovnat
Zkoumat EKSODO 26:33
Domů
Bible
Plány
Videa