Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Yoh. 2

1

Yoh. 2:11

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adaonetsa chizindikiro chake choyambachi m'mudzi wa Kana m'dera la Galileya. Pamenepo adaonetsa ulemerero wake, ndipo ophunzira ake adamkhulupirira.

Compara

Explorar Yoh. 2:11

2

Yoh. 2:4

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adayankha kuti, “Mai, kodi mukuti nditani? Nthaŵi yangatu siinafike.”

Compara

Explorar Yoh. 2:4

3

Yoh. 2:7-8

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Yesu adauza anyamata aja kuti, “Dzazani mbiyazi ndi madzi.” Ndipo adazidzaza mpaka m'milomo. Pambuyo pake adaŵauza kuti, “Tsopano tungani, kaperekeni kwa mkulu wa phwando,” Iwowo adakaperekadi.

Compara

Explorar Yoh. 2:7-8

4

Yoh. 2:19

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adaŵayankha kuti, “Gwetsani nyumba ya Mulungu ino, Ine ndidzaimanganso masiku atatu.”

Compara

Explorar Yoh. 2:19

5

Yoh. 2:15-16

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Apo Yesu adapanga mkwapulo wazingwe nayamba kuŵatulutsira onse kunja, pamodzi ndi nkhosa ndi ng'ombe zao zomwe. Adagubudula matebulo a osinthitsa ndalama aja, naŵamwazira ndalama zao. Ndipo adalamula ogulitsa nkhunda aja kuti, “Izi zitulutseni muno. Nyumba ya Atate anga musaisandutse nyumba yochitiramo malonda.”

Compara

Explorar Yoh. 2:15-16

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Yoh. 2

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Inici

La Bíblia

Plans

Vídeos