Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Marko 15

1

Marko 15:34

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pa ora lachisanu ndi chinayi Yesu analira mofuwula kuti, “Eloi, Eloi, lama sabakitani?” Kutanthauza kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?”

Compara

Explorar Marko 15:34

2

Marko 15:39

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Kenturiyo, amene anayima patsogolo pa Yesu, atamva kulira kwake ndi kuona mmene anafera anati, “Zoonadi, uyu anali Mwana wa Mulungu.”

Compara

Explorar Marko 15:39

3

Marko 15:38

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Chinsalu chotchinga cha mʼNyumba ya Mulungu chinangʼambika pakati kuyambira pamwamba mpaka pansi.

Compara

Explorar Marko 15:38

4

Marko 15:37

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndi mawu ofuwula, Yesu anapuma komaliza.

Compara

Explorar Marko 15:37

5

Marko 15:33

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pa ora lachisanu ndi chimodzi masana mdima unabwera pa dziko lonse mpaka pa ora lachisanu ndi chinayi masana.

Compara

Explorar Marko 15:33

6

Marko 15:15

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pilato pofuna kuwakondweretsa anthuwo, anawamasulira Baraba. Analamula kuti Yesu akwapulidwe mwankhanza, ndipo anamupereka kuti akapachikidwe.

Compara

Explorar Marko 15:15

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Marko 15

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest