Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Mateyu 20

1

Mateyu 20:26-28

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Siziyenera kutero ndi inu. Mʼmalo mwake, aliyense amene akufuna kukhala wamkulu pakati panu akhale wotumikira wanu. Ndipo aliyense amene akufuna kukhala woyamba akhale kapolo wanu. Momwenso Mwana wa Munthu sanabwere kudzatumikiridwa, koma kudzatumikira, ndi kupereka moyo wake kukhala dipo la anthu ambiri.”

Compara

Explorar Mateyu 20:26-28

2

Mateyu 20:16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Momwemo omalizira adzakhala oyamba ndipo oyamba adzakhala omalizira.”

Compara

Explorar Mateyu 20:16

3

Mateyu 20:34

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anamva nawo chifundo ndipo anakhudza maso awo. Nthawi yomweyo anaona namutsata Iye.

Compara

Explorar Mateyu 20:34

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Mateyu 20

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest