1
Hoseya 7:14
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Iwo salirira kwa Ine kuchokera pansi pa mtima, koma amalira mofuwula ali pa bedi pawo. Amadzichekacheka chifukwa chofuna tirigu ndi vinyo watsopano, koma amandifulatira.
Compara
Explorar Hoseya 7:14
2
Hoseya 7:13
Tsoka kwa iwo, chifukwa andisiya Ine! Chiwonongeko kwa iwo, chifukwa andiwukira! Ndimafunitsitsa kuwapulumutsa koma amayankhula za Ine monama.
Explorar Hoseya 7:13