1
Hoseya 2:19-20
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya; ndidzakutomera mwachilungamo, mwaungwiro, mwachikondi ndi mwachifundo. Ndidzakutomera mokhulupirika ndipo udzadziwa Yehova.
Compara
Explorar Hoseya 2:19-20
2
Hoseya 2:15
Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa, ndipo ndidzasandutsa Chigwa cha Akori kukhala khomo la chiyembekezo. Kumeneko iye adzayimba nyimbo monga mʼmasiku a ubwana wake, monga tsiku limene anatuluka ku Igupto.
Explorar Hoseya 2:15