Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Amosi 5

1

Amosi 5:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi, chilungamo ngati mtsinje wosaphwa!

Compara

Explorar Amosi 5:24

2

Amosi 5:14

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa, kuti mukhale ndi moyo. Mukatero Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzakhala nanu, monga mmene mumanenera kuti ali nanu.

Compara

Explorar Amosi 5:14

3

Amosi 5:15

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino; mukhazikitse chiweruzo cholungama mʼmabwalo anu amilandu. Mwina mwake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzachitira chifundo anthu otsala a mʼbanja la Yosefe.

Compara

Explorar Amosi 5:15

4

Amosi 5:4

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi: “Mundifunefune kuti mukhale ndi moyo

Compara

Explorar Amosi 5:4

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest