YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

YOHANE 9 的热门经文

1

YOHANE 9:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.

对照

探索 YOHANE 9:4

2

YOHANE 9:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.

对照

探索 YOHANE 9:5

3

YOHANE 9:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.

对照

探索 YOHANE 9:2-3

4

YOHANE 9:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.

对照

探索 YOHANE 9:39

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频