YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 19 的热门经文

1

GENESIS 19:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

对照

探索 GENESIS 19:26

2

GENESIS 19:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake akazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mudzi.

对照

探索 GENESIS 19:16

3

GENESIS 19:17

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.

对照

探索 GENESIS 19:17

4

GENESIS 19:29

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo panali pamene Mulungu anaononga midzi ya m'chigwa, Mulungu anakumbukira Abrahamu, natulutsa Loti pakati pa chionongeko, pamene anaononga midzi m'mene anakhalamo Loti.

对照

探索 GENESIS 19:29

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频